18. Akuwapanga adzafanana nao;Inde, onse akuwakhulupirira.
19. A nyumba ya Israyeli inu, lemekezani Yehova:A nyumba ya Aroni inu, lemekezani Yehova:
20. A nyumba ya Levi inu, lemekezani Yehova:Inu akuopa Yehova, lemekezani Yehova.
21. Alemekezedwe Yehova kucokera m'Ziyoni,Amene akhala m'Yerusalemu.Haleluya,