6. Makutu ali nao, koma osamva;Mphuno ali nazo, koma osanunkhiza;
7. Manja ali nao, koma osagwira;Mapazi ali nao, koma osayenda;Kapena sanena pammero pao,
8. Adzafanana nao iwo akuwapanga;Ndi onse akuwakhulupirira,
9. Israyeli, khulupirira Yehova:Ndiye mthandizi wao ndi cikopa cao.