2. Ndipo Yuda anaona kumeneko mwana wamkazi wa Mkanani dzina lace Sua: ndipo anamtenga, nalowa kwa iye.
3. Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namucha dzina lace Eri.
4. Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namucha dzina lace Onani.