14. Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.
15. Ana a Adini, mazana anai mphambu makumi asanu kudza anai.
16. Ana a Ateri, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi atatu.
17. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.
18. Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.
19. Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
20. Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.
21. Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.
22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.