27. Anatumiza kwa iwo a ku Beteli, ndi kwa iwo a ku Ramoti wa kumwela, ndi kwa iwo a ku Yatiri;
28. ndi kwa iwo a ku Aroeri, ndi kwa iwo a ku Sifimoti, ndi kwa iwo a ku Estimoa;
29. ndi kwa iwo a ku Rakala, ndi kwa iwo a m'midzi ya Ayerameli, ndi kwa iwo a m'midzi ya Akeni;
30. ndi kwa iwo a ku Horima, ndi kwa iwo a ku Korasani, ndi kwa iwo a ku Ataki;
31. ndi kwa iwo a ku Hebroni, ndi kumalo konse kumene Davide ndi anthu ace adafoyendayenda.